Author: TV Islam Malawi
-

CDEDI Says Shop Closures could Destabilize the Country’s Economy.
Centre for Democracy and Economic Development Initiatives (CDEDI) has intensified pressure on business operators resisting the Malawi Revenue Authority’s newly introduced Electronic Invoicing System (EIS), warning that continued shop closures could destabilize the country’s economy. The Electronic Invoicing System, which officially replaced Electronic Fiscal Devices on May 1, 2026, was introduced by the Malawi Revenue…
-

“Kutsika Mtengo Kwa Petrol, Kuthandiza Kukhazikika Kwa Mitengo Ya Katundu,” Watero Katswiri Waza Chuma.
Katswiri pa nkhani za chuma, Christopher Mbukwa, wati kutsika kwa mtengo wa mafuta a Petrol kuthandiza kukhazikika kwa mitengo ya katundu yomwe yakhala ikukwera. Poyankhula ndi TVI, a Mbukwa ati kutsika kwa mtengo wa mafuta ndi chimodzi mwa zipatso zabwino za ndondomeko ya Automatic Fuel Pricing Mechanism. Iwo ati ndi ndondomekoyi, anthu ambiri amayembekezera kuti…
-
“Inspect Gas Equipment Before Use,” Police Advise.
Police in Mangochi have advised members of the public who use cooking gas cylinders to regularly inspect their gas equipment before use. The advise follows an incident involving a 21-year-old woman identified as Neliya Aufi who has been hospitalized at Mangochi District Hospital after sustaining burns when a cooking gas cylinder exploded while she was…
-

“Addressing Labor Challenges can Ensure Decent Work,” Minister.
Minister of Labour, Skills and Innovation, Joel Chigona, says Malawi’s efforts to achieve decent work will depend on how quickly the country addresses ongoing labour challenges. Speaking during a press briefing on Wednesday ahead of Labour Day celebrations at Masintha Ground, Chigona said unemployment, low wages, delayed salaries and limited social protection remain major concerns…
-

Police Arrest 15 Fuel Vendors
Police in Mzuzu have on Tuesday, arrested 13 suspects for being found in possession of petroleum products without license and other offences. Assistant Public Relations Officer for Mzuzu Police Station, Sergeant Edson Chipeni, says the suspects were arrested during a simultaneous intelligence driven operation, aimed at curbing criminal activities in the city. According to Chipeni,…
-

“Ogwira Ntchito Adzitetezeka Pa Ntchito,” yatero MEHA.
Bungwe la Malawi Environmental Health Association (MEHA) lalangiza olemba ntchito mdziko muno kuti awonetsetse kuti malo awo ogwilira ntchito akuthandizira kupititsa patsogolo umoyo wa ogwira ntchito powateteza ku ngozi komanso matenda osiyanasiyana.Mtsogoleri wa bungwe la MEHA, Bertha Sato, walankhula izi Lachisanu, pamene dziko lonse likukumbukira tsiku loona za chitetezo ndi umoyo wabwino m’malo ogwira ntchito,…
